N’ciani Catsopano?
NYIMBO ZOPEKEDWA KOYAMBA
“Uthenga Wabwino”! (Nyimbo ya pa Msonkhano Wacigawo wa 2024)
Kuyambila m’zaka za zana loyamba mpaka masiku ano, mwacimwemwe anthu akhala akulalikila uthenga wabwino. Uthengawo ni wofunika kwambili kuposa uthenga wina ulionse cifukwa umakamba za nchito imene Yesu iye mwini anaiyambitsa, komanso mmene angelo amamuthandizila pa nchitoyi.
NSANJA YA MLONDA
Kodi Tingawapeze Kuti Malangizo Odalilika
Onani mmene mungapangile zisankho zabwino zimene zidzakuthandizani limodzi na banja lanu kukhala na tsogolo labwino.
KHALANI MASO!
Kodi Nkhondo Zidzatha Liti?—Kodi Baibo Ikutipo Ciyani?
Posacedwa, nkhondo zonse zidzatha. Baibo imafotokoza mmene nkhondo zidzathela.
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Zimene Zingakuthandizeni Mukasamukila mu Mpingo Watsopano
Akhristu ambili akwanitsa kuzoloŵela mpingo watsopano. N’ciyani cimathandiza munthu kuzoloŵela mpingo watsopano? Onani mfundo zinayi zimene zingakuthandizeni.
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga—July 2024
Kodi “mkazi” wochulidwa pa Yesaya 60:1 ndani, nanga ‘adzaimilila’ motani, ndipo ‘adzaonetsa kuwala kwake’ motani?
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
Khalanibe Maso mwa Kuŵelenga Baibo Mwakhama
NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA
July 2024
Magazini ino ili na nkhani zophunzila mu mlungu wa September 9–October 6, 2024.