Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Anzanu

Anzanu

Chigawo 3

Anzanu

Kodi mumaona kuti kukhala ndi anzanu n’kofunika?

□ N’kosafunika

□ N’kosafunika kwenikweni

□ N’kofunika kwambiri

Kodi mumavutika kupeza anthu ocheza nawo?

□ Inde

□ Ayi

Kodi muli ndi mnzanu wapamtima?

□ Inde

□ Ayi

Kodi mumafuna kuti mnzanu akhale ndi khalidwe lotani?

Baibulo limati: “Bwenzi limakonda nthawi zonse; ndipo m’bale anabadwira kuti akuthandize pooneka tsoka.” (Miyambo 17:17) Aliyense amafuna kukhala ndi mnzake wotere. Koma kupeza anzanu abwino n’kovuta. Kodi mungatani kuti mupeze anzanu abwino ndiponso kuti muzigwirizana nawo bwinobwino? Onani malangizo amene ali m’Mitu 9 mpaka 12.

[Chithunzi chachikulu pamasamba 84, 85]