Phunzitsani Ana Anu
Makolo, gwiritsani ntchito nkhanizi pophunzitsa ana anu mfundo zofunika kwambiri za m’Baibulo.
Mawu Oyamba
Mawu a m’buku la Deuteronomo angakuthandizeni polera ana.
PHUNZIRO
Chinsinsi Chimene Tonsefe Timafuna Titachidziwa
Baibulo limanena kuti pali nkhani inayake yachinsinsi ndipo limati nkhani imeneyi ndi “chinsinsi chopatulika.” Kodi ukufuna kudziwa chinsinsi chimenechi?
PHUNZIRO
Rabeka Ankafuna Kusangalatsa Yehova
Kodi tingatani kuti tifanane ndi Rabeka? Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zambiri.
PHUNZIRO
Rahabi Ankakhulupirira Yehova
Werengani nkhaniyi kuti mmene Rahabi ndi abale ake anapulumukira pamene mzinda wa Yeriko unkawonongedwa.
PHUNZIRO
Anasangalatsa Bambo Ake Komanso Yehova
Kodi mwana wa Yefita ana anakwaniritsa lonjezo liti? Kodi tingatani kuti titsatire chitsanzo chake?
PHUNZIRO
Samueli Anapitiriza Kuchita Zinthu Zabwino
Kodi mungatsanzire bwanji chitsanzo cha Samueli?
PHUNZIRO
Davide Sankachita Mantha
Werengani nkhaniyi m’Baibulo kuti mudziwe zimene zinamuthandiza Davide kuti akhale wolimba mtima.
PHUNZIRO
Kodi Nthawi Zina Umaona Kuti Uli Wekha?
Kodi Yehova anauza chiyani Eliya atayamba kumva ngati kuti watsala yekha? Kodi mukuphunzirapo chiyani pa zimene zinachitikira Eliya?
PHUNZIRO
Yosiya Anali ndi Anzake Abwino
Baibulo limatiuza kuti zinali zovuta kwambiri kwa mnyamata wina, dzina lake Yosiya, kuti achite zinthu zabwino. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe mmene anzake a Yosiya anamuthandizira kuti azichita zinthu zabwino.
PHUNZIRO
Yeremiya Sanasiye Kulankhula za Yehova
Ngakhale kuti anthu ankaseka Yeremiya komanso kumukwiyira, n’chifukwa chiyani anapitirizabe kulankhula za Mulungu?
PHUNZIRO
Yesu Anali Womvera
Nthawi zina kumvera n’kovuta. Werengani nkhaniyi kuti muone mmene chitsanzo cha Yesu chingakuthandizireni.
PHUNZIRO
Analemba za Yesu
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe za anthu 8 omwe analemba Baibulo omwe anakhala ndi moyo m’nthawi imenenso Yesu anali padziko lapansi ndipo analemba za moyo wa Yesuyo.
PHUNZIRO
Mwana wa Mchemwali wake wa Paulo Anali Wolimba Mtima
Zimene anachitazo zinapulumutsa moyo wa ankolo ake. Kodi mukudziwa zimene anachita?
PHUNZIRO
Timoteyo Ankafuna Kuthandiza Anthu
Kodi iweyo ungatani kuti ukhale ndi moyo wosangalala ngati Timoteyo?
PHUNZIRO
Ufumu Umene Udzalamulira Dziko Lonse
Kodi zinthu zidzakhala bwanji Yesu akadzayamba kulamulira dziko lapansi? Kodi mukufuna kudzaona zimene zidzachitike pa nthawi imeneyo?