GALAMUKANI! January 2013 | Mmene Mungalerere Ana Anu Kuti Asakhale Odzikonda
Mmene tingapewere zinthu zitatu zimene makolo ena amalakwitsa polera ana.
Zochitika Padzikoli
Werengani kuti mudziwe nkhani zomwe zikuchitika m’madera osiyanasiyana padziko lapansi.
MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA
Zimene Mungachite Kuti Muzimasukirana ndi Mwana Wanu
Kodi mumakhumudwa kwambiri chifukwa cholephera kulankhulana bwino ndi mwana wanu? Kodi n’chiyani chimene chimachititsa kuti muzivutika kulankhulana naye?
KUCHEZA NDI ANTHU
Wasayansi Akufotokoza za Chikhulupiriro Chake
Werengani kuti mumve mfundo za sayansi zimene anagwiritsa ntchito komanso chifukwa chake amakhulupirira Mawu a Mulungu.
NKHANI YAPACHIKUTO
Mmene Mungalerere Ana Anu Kuti Asakhale Odzikonda
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe njira zitatu zimene zingathandize kuti ana anu asakhale odzikonda.
ANTHU NDI MAYIKO
Dziko la Cameroon
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe mbiri komanso chikhalidwe cha anthu a ku Cameroon.
ZIMENE BAIBULO LIMANENA
Paradaiso
Kodi Paradaiso adzakhala kumwamba kapena padziko lapansi pompano? Kodi ndani amene andzakhale m’Paradaiso?
KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?
Mbalame Yotha Kuuluka Ulendo Wautali
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe za mbalame inayake yogometsa kwambiri imene imayenda ulendo wautali masiku 8 okha.
Zina zimene zili pawebusaiti
Kodi Ndizitani Ngati Ena Akundichitira Zachipongwe?
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe tanthauzo la kuchitiridwa zachipongwe komanso zimene mungachite ngati mutachitiridwa zachipongwezo.
Solomo Anachita Zinthu Mwanzeru
Pezani zimene zikusowa pachithunzichi, lumikizani timadonthoti ndipo chikongoletseni ndi chekeni.