NSANJA YA OLONDA Na. 6 2016 | Masomphenya Otithandiza Kumvetsa za Kumwamba

Baibulo lingakuthandizeni kudziwa za zinthu zosaoneka.

NKHANI YAPACHIKUTO

Mafunso Okhudza Mmene Zilili Kumwamba

Tikhoza kupeza mayankho odalirika a mafunso okhudza kumwamba.

NKHANI YAPACHIKUTO

Masomphenya Osonyeza Amene Ali Kumwamba

Kodi Malemba amanena zotani zokhudza Yehova Mulungu, Yesu Khristu ndiponso angelo okhulupirika?

Zimene Tingaphunzire kwa Mbalame

Mbalame zimasonyeza kuti Mulungu ndi mlengi wanzeru komanso zimatithandiza kuganizira zinthu zofunika kwambiri.

Lefèvre d’Étaples Ankafuna Kuti Anthu Wamba Adziwe Mawu a Mulungu

Kodi anakwanitsa bwanji kumasulira Baibulo m’Chifulenchi ngakhale kuti ankatsutsidwa?

MBIRI YA MOYO WANGA

Ndilibe Manja Koma Ndinatha Kulandira Choonadi cha M’Baibulo

Mnyamata wina amene anachita ngozi yoopsa anapeza umboni womuthandiza kukhulupirira kuti kuli Mulungu.

Kodi Baibulo Limanena Zotani?

Kodi Mulungu amamvetsera ndiponso kuyankha mapemphero anu?

Zina zimene zili pawebusaiti

Kodi Mulungu Analenga Mdyerekezi Kuti Azitiyesa?

Kodi Satana anachokera kuti? Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake Yesu ananena kuti Mdyerekezi “sanakhazikike m’choonadi.”