BAIBULO LIMASINTHA ANTHU
Juan Pablo Zermeño: Yehova Anandithandiza Kukhala ndi Moyo Watanthauzo
Anthu ambiri amakhala ndi moyo wamtendere komanso watanthauzo akadzipereka kwa Yehova ngakhale kuti anakumana ndi mavuto akuluakulu ali ana. Juan Pablo anasankha kusiya masewera a nkhonya ndipo panopa akukhala moyo watanthauzo.